CMD

MWAZIZIWA? > Articles by: CMD

KUGULISA MWANA NGATI MBUZI PA MTENGO WA K2,000,000

Eeeh koma KUTI mumve inuyo izi mmmh! Zimene zachitika ku South Africa zili ngati nthano komanso maloto. Akuti Mayi wina dzina lake Racquel “Kelly” Smith wachita zachilendo kwambiri, mpaka ma Judge owelura sanakhulupirire izi atamva. Mai uyu anagulitsa mwana wake wa zaka 6, dzina lake Joshlin, ngati akugulitsa nsima pamsika! Ndipo kuyimvetsetsa bwino nkhaniyi, akuti…

Read More
Woman-charged-with-manslaughter-in-fatal-jet-ski-collision

NKHANI YOKUPHA MWANA NDI KUTHAWA

Mtsikana wachichepele dzina lake Ava Moore, yemwe anali ndi zaka 18 zokha, anamwalira atagundidwa ndi jet ski pamene anali kosangalala m’nyanja. Izi zinachitika kumapeto kwa sabata m’nyanja imene ili ku Texas. Mayi wina wazaka 21, dzina lake Daikerlyn Gonzalez, ndiye amene anali kuyendetsa jet ski. Uyu ndi wochokera ku Venezuela ndipo analowa m’dziko popanda zikalata…

Read More
MISS MALAWI 2025

BEAUTY CONTEST – MA MISS MALAWI A ULENDO UNO AKONGOLA ZA MWANO

Asungwana okwana khumi ndi anayi ndi omwe akhale akukathambitsana mu mpikisano wa chaka chino wa ziphadzuwa zolimbikitsa chikhalidwe wa Miss Culture Malawi. Mokonzedwa ndi a Lush Africa Foundation, mpikisanowu uchitika pa 29 November ku BICC mu mzinda wa Lilongwe. Asungwanawa ndi Leonorah Cooke, Lutondwa Mwenifumbo, Michelle Mwanamai, Natasha Kwaela, Mtendele Chimango, Mellisah Kamangira, Thokozani Lupoka,…

Read More
Theresa phodo ndi Praise Umali

PALIBE CHINSISI ZAZIWIKA LERO ZA ANTHU AWA

Iyi si miseche koma chilungamo cha nkhani. Praise Umali ndi Mkazi uyu Thereza Phodo abwela poyela sanafune abise mpaka kale. Monga mukudziwa za woyimba awa samadziwika mmene ankalowa mu gulu la Zathu ndi anzawo ena anayi. Koma adachilimika mpaka kuzama mu zisudzo komanso maimbidwe kufikira pomwe gulu la Zathu linazilala.Pano aluso wonse asanu ndi mmodzi…

Read More
MURDERED WIFE

KODI NDI ZA KUCHIPINDA ZOMWE UYU WAPHELA MKAZI WAKE?

Koma abale zina ukamva mmmh, Akuti Ku Chiradzulu apolisi amanga a Dyson Makawa powaganizila kuti apha mkazi wawo atasemphana pa nkhani zam’banja. Mneneri wa polisi m’bomali, a Cosmas Kagulo awuza Zodiak Online lero kuti a Makawa akuganiziridwa kuti anapha mkazi wawo Zione John yemwe anasiyana nayo atasemphana maganizo. Iwo ati pa 17 mwezi uno a…

Read More

WHY? Illovo Sugar Malawi Has partnered with the Ministry of Trade.

Illovo Sugar Malawi has reaffirmed its commitment to ensuring the availability of sugar on the local market by partnering with the Ministry of Trade and national security agencies to curb illegal sugar exports to neighbouring countries. This initiative aims to protect domestic consumers from artificial shortages and price instability. Acting Managing Director Kondwani Msimuko disclosed…

Read More
Mzimba

MZIMBA NAYO YATI CHUMA CHATHU OSACHITA NACHO ZOPUSA

Mwaziva? Mzimba si ya anthu ogona ayi. Akana zokuti ndalama za CDF azisunga ndi anduna. Nkhani ikuti, Citizens and civil society groups in Mzimba have welcomed the recent constitutional court decision that strips Members of Parliament (MPs) of direct control over the Constituency Development Fund (CDF). The ruling is being praised as a progressive move…

Read More