MWAZIZIWA? > ZINA UKAMVA

KUTUKWANISA CHAKWERA OSALAKWA UKU ~ MBAVA ZA AZIMAYI AZIPANGA IZI KU LILONGWE KWA MCP

MWAIMVA? Akutitu apolisi ku Lilongwe amanga amayi atatu omwe akuwaganizira kuti mothandizidwa ndi anthu ena anathyola mnyumba ndikubamo katundu monga deep freezer, upright fridge, mattress, microwave ndi katundu wina. Amayiwa, malinga ndi mneneri wa polisi a Hastings Chigalu ndi a Chimwemwe Chembe a zaka 39, a Elizabeth Mkwezalamba a zaka 36 komanso a Memory Elias…

Read More

KUZIZILA UKU ANA AGONE KU POLICE ZOONA?

Four (4) students were recently arrested at Mikundi School in Mchinji for exchanging answers during an examination. According to Dorothy Nampota, Executive Director of the Malawi National Examinations Board (MANEB), the students were caught swapping papers while the exams were ongoing. She added that despite this incident, the examinations are generally progressing well, with 257,129…

Read More

KOMA ABALE MUNTHU KUMUTELE ZOONA?

Kodi apapa nde tinene kuti kwayambika zotani nanga? Akuti apolisi m’boma la Mulanje akusakasaka anthu omwe apha ndikuotcha a Luka Saluwa a zaka 35 kaamba koti amawaganizira kuti anapha mayi Rita Maluku a zaka 43 ochokera kwa Misomali Kwa mfumu yaikulu Chikumbu m’boma la Mulanje. M’neneri wapolisi ya m’bomali a Innocent Moses ati lachitatu sabata…

Read More