KOMA AWAWA ANGANENE IZI KUCHIPINDA KWA MCP CHAKWERA AKUMVA?
Mwaimva? Akutitu wachiwiri kwa mtsogoleri wachipani cha Peoples PP, mchigawo chapakati, a Peter Kamange, auza anthu ku Mchinji kuti chipanichi motsogozedwa ndi mtsogoleri wake a Joyce Banda ndiwokonzeka kuthetsa mavuto azachuma omwe ali mdziko muno pano miyezi isanu ndi umodzi yokha atangotenga boma. A Kamange , anena izi pamsonkhano omwe anachititsa pa bwalo la Magawa….