KWAYAMBIKA NKHONDO YOMENYELANA MISONKHO YATHU KU BOMA
Mwaziziwa? Ndalama zathu amalawi zikufunika kuzisalira kudya zinthu sizili bwino. Nanga tangoganizani , akuti mlangizi wa boma pa za malamulo a Thabo Chakaka Nyirenda ati atengera chigamulo cha bwalo la zamalamulo (Constitutional Court) chokhudza kagwiritsidwe ntchito ka ndalama za chitukuko za CDF ku Bwalo lalikulu la Supreme. A Nyirenda awuza Times kuti apita ku bwaloli…