...
MWAZIZIWA? >
CHIMWENDO BANDA

KOMA CHIMWENDO AZASIYA BOZA LAKE LIJA? TAMUMVENI ZOMWE WAUZA ANTHU UKU.

Malawi Congress Party (MCP) Secretary General Richard Chimwendo Banda has said President Lazarus Chakwera is the only presidential candidate in the September 16 general elections who truly prioritizes the development of the nation. Speaking at a political rally held at Chatata Ground in Lilongwe City Central Constituency, Chimwendo Banda emphasized that President Chakwera has already…

Read More
People's party

KOMA AWAWA ANGANENE IZI KUCHIPINDA KWA MCP CHAKWERA AKUMVA?

Mwaimva? Akutitu wachiwiri kwa mtsogoleri wachipani cha Peoples PP, mchigawo chapakati, a Peter Kamange, auza anthu ku Mchinji kuti chipanichi motsogozedwa ndi mtsogoleri wake a Joyce Banda ndiwokonzeka kuthetsa mavuto azachuma omwe ali mdziko muno pano miyezi isanu ndi umodzi yokha atangotenga boma. A Kamange , anena izi pamsonkhano omwe anachititsa pa bwalo la Magawa….

Read More
Seraphinite AcceleratorOptimized by Seraphinite Accelerator
Turns on site high speed to be attractive for people and search engines.