PALIBE CHINSISI ZAZIWIKA LERO ZA ANTHU AWA
Iyi si miseche koma chilungamo cha nkhani. Praise Umali ndi Mkazi uyu Thereza Phodo abwela poyela sanafune abise mpaka kale. Monga mukudziwa za woyimba awa samadziwika mmene ankalowa mu gulu la Zathu ndi anzawo ena anayi. Koma adachilimika mpaka kuzama mu zisudzo komanso maimbidwe kufikira pomwe gulu la Zathu linazilala.Pano aluso wonse asanu ndi mmodzi…